Masalimo 135:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo anapereka dziko lao likhale cholowa, cholowa cha kwa Israele anthu ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo anapereka dziko lao likhale chosiyira, chosiyira cha kwa Israele anthu ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Adapereka dziko lao kuti likhale choloŵa, choloŵa cha Aisraele, anthu ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 ndipo anapereka dziko lawo ngati cholowa, cholowa cha anthu ake Aisraeli. Onani mutuwo |