Masalimo 132:9 - Buku Lopatulika9 Ansembe anu avale chilungamo; ndi okondedwa anu afuule mokondwera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ansembe anu avale chilungamo; ndi okondedwa anu afuule mokondwera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Ansembe anu avale chilungamo ngati nsalu, anthu anu oyera mtima afuule ndi chimwemwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ansembe anu avekedwe chilungamo; anthu anu oyera mtima ayimbe nyimbo mwachimwemwe.’ ” Onani mutuwo |