Masalimo 132:14 - Buku Lopatulika14 Pampumulo panga mpano posatha, Pano ndidzakhala; pakuti ndakhumbapo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Pampumulo panga mpano posatha, Pano ndidzakhala; pakuti ndakhumbapo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Akuti, “Ameneŵa ndiwo malo anga opumuliramo mpaka muyaya. Ndidzakhala kuno chifukwa ndakufunitsitsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 “Awa ndi malo anga opumapo ku nthawi za nthawi; ndidzakhala pano pa mpando waufumu, pakuti ndakhumba zimenezi. Onani mutuwo |