Masalimo 132:15 - Buku Lopatulika15 Ndidzadalitsatu chakudya chake; aumphawi ake ndidzawakhutitsa ndi mkate. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndidzadalitsatu chakudya chake; aumphawi ake ndidzawakhutitsa ndi mkate. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 “Ndidzadalitsa kwambiri mzinda wa Ziyoni poupatsa zosoŵa zake, anthu ake osauka, ndidzaŵapatsa chakudya chokwanira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Ndidzadalitsa mzindawu ndi zinthu zambiri; anthu ake osauka ndidzawakhutitsa ndi chakudya. Onani mutuwo |