Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 132:13 - Buku Lopatulika

13 pakuti Yehova anasankha Ziyoni; analikhumba likhale pokhala pake; ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 pakuti Yehova anasankha Ziyoni; analikhumba likhale pokhala pake; ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Chauta wasankhula Ziyoni, akufuna kuti akhale malo ake okhalamo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Pakuti Yehova wasankha Ziyoni, Iye wakhumba kuti akhale malo ake okhalamo:

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 132:13
11 Mawu Ofanana  

komatu sindidzachotsa ufumu wonsewo; fuko limodzi ndidzapatsa mwana wako, chifukwa cha Davide mtumiki wanga, ndi chifukwa cha Yerusalemu amene ndinamsankha.


Pakuti ndasankha ndi kuipatula nyumba iyi, kuti dzina langa likhaleko chikhalire; inde maso anga ndi mtima wanga zidzakhala komweko kosalekeza.


Aliyense mwa inu a anthu ake onse, Mulungu wake akhale naye, akwere kunka ku Yerusalemu, ndiwo mu Yuda, nakaimange nyumba ya Yehova Mulungu wa Israele; Iye ndiye Mulungu wokhala mu Yerusalemu.


Muchitiranji nsanje mapiri inu a mitumitu, ndi phirilo Mulungu analikhumba, akhaleko? Inde, Yehova adzakhalabe komweko kosatha.


Yehova akonda zipata za Ziyoni koposa zokhalamo zonse za Yakobo.


Pakuti Iye wofuna chamwazi awakumbukira; saiwala kulira kwa ozunzika.


Ndipo adzayankhanji amithenga a amitundu? Kuti Yehova wakhazikitsa Ziyoni, ndipo m'menemo anthu ake ovutidwa adzaona pobisalira.


Komatu mwayandikira kuphiri la Ziyoni, ndi mzinda wa Mulungu wamoyo, Yerusalemu wa Kumwamba, ndi kwa unyinji wochuluka wa angelo,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa