Masalimo 132:13 - Buku Lopatulika13 pakuti Yehova anasankha Ziyoni; analikhumba likhale pokhala pake; ndi kuti, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 pakuti Yehova anasankha Ziyoni; analikhumba likhale pokhala pake; ndi kuti, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Chauta wasankhula Ziyoni, akufuna kuti akhale malo ake okhalamo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Pakuti Yehova wasankha Ziyoni, Iye wakhumba kuti akhale malo ake okhalamo: Onani mutuwo |