Masalimo 132:11 - Buku Lopatulika11 Yehova analumbira Davide zoona; sadzalibweza; ndi kuti, Wa iwo okhala zipatso za thupi lako ndidzaika pa mpando wachifumu wako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Yehova analumbira Davide zoona; sadzalibweza; ndi kuti, Wa iwo okhala zipatso za thupi lako ndidzaika pa mpando wachifumu wako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Chauta adalumbirira Davide momtsimikizira, ndipo sadzasintha, adati, “Ndidzakhazika pa mpando wachifumu mmodzi mwa ana ako aamuna. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Yehova analumbira kwa Davide, lumbiro lotsimikizika kuti Iye sadzasintha: “Mmodzi wa ana ako ndidzamuyika pa mpando waufumu; Onani mutuwo |