Masalimo 132:12 - Buku Lopatulika12 Ana ako akasunga chipangano changa ndi mboni yanga imene ndidzawaphunzitsa, ana aonso adzakhala pa mpando wanu kunthawi zonse, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ana ako akasunga chipangano changa ndi mboni yanga imene ndidzawaphunzitsa, ana aonso adzakhala pa mpando wanu kunthawi zonse, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Ngati ana ako aamuna asunga chipangano changa ndi malamulo anga amene ndidzaŵaphunzitsa, ana aonso adzakhala pa mpando wako wachifumu mpaka muyaya.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 ngati ana ako azisunga pangano langa ndi malamulo amene ndiwaphunzitsa, pamenepo ana awo adzakhala pa mpando wako waufumu kwamuyaya ndi muyaya.” Onani mutuwo |