Masalimo 129:3 - Buku Lopatulika3 Olima analima pamsana panga; anatalikitsa mipere yao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Olima analima pamsana panga; anatalikitsa mipere yao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 “Pondikwapula adani anga adachita ngati kulima pamsana panga, kulima mizere yaitali.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Anthu otipula analima pa msana panga ndipo anapangapo mizere yayitali: Onani mutuwo |