Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 129:4 - Buku Lopatulika

4 Yehova ndiye wolungama; anadulatu zingwe za oipa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Yehova ndiye wolungama; anadulatu zingwe za oipa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Koma Chauta ndi wolungama, wandimasula zingwe za anthu oipa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Koma Yehova ndi wolungama; Iye wandimasula ku zingwe za anthu oyipa.”

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 129:4
9 Mawu Ofanana  

Yehova Mulungu wa Israele, Inu ndinu wolungama, popeza tinatsala opulumuka monga lero lino; taonani, tili pamaso panu m'kupalamula kwathu; pakuti palibe wakuima pamaso panu chifukwa cha ichi.


Koma Inu ndinu wolungama mwa zonse zatigwera; pakuti mwachita zoona, koma ife tachita choipa;


Inu ndinu wolungama, Yehova, ndipo maweruzo anu ndiwo olunjika.


Akapanda kutembenuka munthu, iye adzanola lupanga lake; wakoka uta wake, naupiringidza.


Yehova ali wolungama; pakuti ndapikisana ndi m'kamwa mwake; mumvetu, mitundu ya anthu nonsenu, nimuone chisoni changa; anamwali ndi anyamata anga atha kulowa m'ndende.


Chifukwa chakusathedwa ife ndicho chifundo cha Yehova, pakuti chisoni chake sichileka,


Ambuye, chilungamo ncha Inu, koma kwa ife manyazi a nkhope yathu, monga lero lino; kwa anthu a Yuda, ndi kwa okhala mu Yerusalemu, ndi kwa Aisraele onse okhala pafupi ndi okhala kutali, kumaiko onse kumene mudawaingira, chifukwa cha kulakwa kwao anakulakwirani nako.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa