Masalimo 129:4 - Buku Lopatulika4 Yehova ndiye wolungama; anadulatu zingwe za oipa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Yehova ndiye wolungama; anadulatu zingwe za oipa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Koma Chauta ndi wolungama, wandimasula zingwe za anthu oipa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Koma Yehova ndi wolungama; Iye wandimasula ku zingwe za anthu oyipa.” Onani mutuwo |