Masalimo 129:2 - Buku Lopatulika2 Anandisautsa kawirikawiri kuyambira ubwana wanga; koma sanandilake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Anandisautsa kawirikawiri kuyambira ubwana wanga; koma sanandilake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Adani akhala akundizunza kwambiri kuyambira unyamata wanga, komabe sadandipambane. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Andizunza kwambiri kuyambira ubwana wanga, koma sanandipambane. Onani mutuwo |