Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 129:2 - Buku Lopatulika

2 Anandisautsa kawirikawiri kuyambira ubwana wanga; koma sanandilake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Anandisautsa kawirikawiri kuyambira ubwana wanga; koma sanandilake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 “Adani akhala akundizunza kwambiri kuyambira unyamata wanga, komabe sadandipambane.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 “Andizunza kwambiri kuyambira ubwana wanga, koma sanandipambane.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 129:2
11 Mawu Ofanana  

Adzakupulumutsa m'masautso asanu ndi limodzi; chinkana mwa asanu ndi awiri palibe choipa chidzakukhudza.


Kundikankha anandikankha ndikadagwa; koma Yehova anandithandiza.


Iwo akukhulupirira Yehova akunga phiri la Ziyoni, losasunthika, likhazikika kosatha.


Masautso a wolungama mtima achuluka, koma Yehova amlanditsa mwa onsewa.


Monga nswala ipuma wefuwefu kukhumba mitsinje; motero moyo wanga upuma wefuwefu kukhumba Inu, Mulungu.


Potero anawaikira akulu a misonkho kuti awasautse ndi akatundu ao. Ndipo anammangira Farao mizinda yosungiramo chuma, ndiyo Pitomu ndi Ramsesi.


Ndiponso Ine ndinena kwa iwe, kuti iwe ndiwe Petro, ndipo pa thanthwe ili ndidzakhazika Mpingo wanga; ndipo makomo a dziko la akufa sadzagonjetsa uwo.


Zinthu izi ndalankhula ndi inu, kuti mwa Ine mukakhale nao mtendere. M'dziko lapansi mudzakhala nacho chivuto, koma limbikani mtima; ndalingonjetsa dziko lapansi Ine.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa