Masalimo 125:3 - Buku Lopatulika3 Pakuti ndodo yachifumu ya choipa siidzapumula pa gawo la olungama; kuti olungama asatulutse dzanja lao kuchita chosalungama. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pakuti ndodo yachifumu ya choipa siidzapumula pa gawo la olungama; kuti olungama asatulutse dzanja lao kuchita chosalungama. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Mafumu oipa sadzalamulira nthaŵi yonse dziko limene lapatsidwa kwa anthu ake, kuti nawonso anthu olungamawo angachite zoipa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Ndodo yaufumu ya anthu oyipa sidzakhala pa dziko limene lapatsidwa kwa anthu olungama, kuti anthu olungamawo angachite nawonso zoyipa. Onani mutuwo |