Masalimo 125:4 - Buku Lopatulika4 Chitirani chokoma, Yehova, iwo okhala okoma; iwo okhala oongoka mumtima mwao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Chitirani chokoma, Yehova, iwo okhala okoma; iwo okhala oongoka mumtima mwao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Chauta, achitireni zabwino anthu amene ali abwino, amene ali olungama mtima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Yehova chitirani zabwino amene ndi abwino, amene ndi olungama mtima Onani mutuwo |