Masalimo 125:2 - Buku Lopatulika2 Monga mapiri azinga Yerusalemu, momwemo Yehova azinga anthu ake, kuyambira tsopano kufikira nthawi zonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Monga mapiri azinga Yerusalemu, momwemo Yehova azinga anthu ake, kuyambira tsopano kufikira nthawi zonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Monga momwe mapiri amazingira Yerusalemu, momwemonso Chauta akuzinga anthu ake kuyambira tsopano mpaka muyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Monga mapiri azungulira Yerusalemu, momwemonso Yehova azungulira anthu ake kuyambira tsopano mpaka muyaya. Onani mutuwo |