Masalimo 125:1 - Buku Lopatulika1 Iwo akukhulupirira Yehova akunga phiri la Ziyoni, losasunthika, likhazikika kosatha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Iwo akukhulupirira Yehova akunga phiri la Ziyoni, losasunthika, likhazikika kosatha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Anthu amene amakhulupirira Chauta ndi olimba ngati phiri la Ziyoni, limene silingathe kugwedezeka, koma ndi lokhala mpaka muyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Amene amadalira Yehova ali ngati phiri la Ziyoni, limene silingagwedezeke koma ndi lokhala mpaka muyaya. Onani mutuwo |