Masalimo 123:1 - Buku Lopatulika1 Ndikweza maso anga kwa Inu, kwa Inu wakukhala kumwamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndikweza maso anga kwa Inu, kwa Inu wakukhala kumwamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Ndikukweza maso anga kwa Inu, Inu amene mumakhala pa mpando wachifumu kumwamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Ndikweza maso anga kwa Inu, kwa Inu amene mumakhala kumwamba. Onani mutuwo |