Masalimo 122:9 - Buku Lopatulika9 Chifukwa cha nyumba ya Yehova Mulungu wathu ndidzakufunira zokoma. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Chifukwa cha nyumba ya Yehova Mulungu wathu ndidzakufunira zokoma. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Chifukwa cha Nyumba ya Chauta, Mulungu wathu, ndidzakupemphera zabwino. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Chifukwa cha Nyumba ya Yehova Mulungu wathu, ndidzakufunira zabwino. Onani mutuwo |