Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 122:8 - Buku Lopatulika

8 Chifukwa cha abale anga ndi mabwenzi anga, ndidzanena tsopano, Mukhale mtendere mwa inu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Chifukwa cha abale anga ndi mabwenzi anga, ndidzanena tsopano, Mukhale mtendere mwa inu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Chifukwa cha abale anga ndi abwenzi anga ndidzanena kuti, “Mtendere ukhaledi m'kati mwako.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Chifukwa cha abale anga ndi abwenzi anga ndidzati, “Mtendere ukhale mʼkati mwako.”

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 122:8
7 Mawu Ofanana  

Ine ndine wakuyanjana nao onse akukuopani, ndi iwo akusamalira malangizo anu.


Za oyera mtima okhala padziko lapansi, iwo ndiwo omveka mbiri, mwa iwowo muli chikondwero changa chonse.


Ndidzikumbukira izi ndipo nditsanulira moyo wanga m'kati mwa ine, pakuti ndinkapita ndi unyinji wa anthu, ndinawatsogolera kunyumba ya Mulungu, ndi mau akuimbitsa ndi kuyamika, ndi unyinji wakusunga dzuwa lokondwera.


ndipo muzitero kwa wodalayo, Mtendere ukhale pa inu, mtendere ukhalenso pa nyumba yanu, ndi mtendere ukhale pa zonse muli nazo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa