Masalimo 122:6 - Buku Lopatulika6 Mupempherere mtendere wa Yerusalemu; akukonda inu adzaona phindu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Mupempherere mtendere wa Yerusalemu; akukonda inu adzaona phindu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Pemphererani mtendere wa Yerusalemu ponena kuti, “Anthu amene amakukonda iwe Yerusalemu, zinthu ziziŵayendera bwino. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Pemphererani mtendere wa Yerusalemu: “Iwo amene amakukonda iwe zinthu ziwayendere bwino. Onani mutuwo |