Masalimo 121:8 - Buku Lopatulika8 Yehova adzasungira kutuluka kwako ndi kulowa kwako, kuyambira tsopano kufikira nthawi zonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Yehova adzasungira kutuluka kwako ndi kulowa kwako, kuyambira tsopano kufikira nthawi zonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Chauta adzakusunga kulikonse kumene udzapita, kuyambira tsopano mpaka muyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Yehova adzayangʼanira kutuluka kwako ndi kulowa kwako; kuyambira tsopano mpaka muyaya. Onani mutuwo |