Masalimo 121:7 - Buku Lopatulika7 Yehova adzakusunga kukuchotsera zoipa zilizonse; adzasunga moyo wako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Yehova adzakusunga kukuchotsera zoipa zilizonse; adzasunga moyo wako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Chauta adzakuteteza ku zoipa zonse, adzasamala moyo wako. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Yehova adzakuteteza ku zoyipa zonse; adzasunga moyo wako. Onani mutuwo |