Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 120:2 - Buku Lopatulika

2 Yehova, landitsani moyo wanga kumilomo ya mabodza, ndi kulilime lonyenga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Yehova, landitsani moyo wanga kumilomo ya mabodza, ndi kulilime lonyenga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Ndimati, “Pulumutseni, Inu Chauta, kwa anthu onama ndi kwa anthu onyenga.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Pulumutseni Yehova ku milomo yabodza, ndi kwa anthu achinyengo.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 120:2
8 Mawu Ofanana  

Mboni za chiwawa ziuka, zindifunsa zosadziwa ine.


Ndipo olungama adzachiona, nadzaopa, nadzamseka, ndi kuti,


Milomo yonama inyansa Yehova; koma ochita ntheradi amsekeretsa.


Pakuti anthu ake olemera adzala ndi chiwawa, ndi okhalamo amanena bodza, ndi lilime lao limachita monyenga m'kamwa mwao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa