Masalimo 120:1 - Buku Lopatulika1 Ndinafuulira kwa Yehova mu msauko wanga, ndipo anandivomereza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndinafuulira kwa Yehova mu msauko wanga, ndipo anandivomereza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Ndimalirira Chauta m'mavuto anga kuti andiyankhe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Ndimafuwulira kwa Yehova mʼmasautso anga, ndipo Iye amandiyankha. Onani mutuwo |