Masalimo 118:26 - Buku Lopatulika26 Wodala wakudzayo m'dzina la Yehova; takudalitsani kochokera m'nyumba ya Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Wodala wakudzayo m'dzina la Yehova; takudalitsani kochokera m'nyumba ya Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Ngwodala amene alikudza m'dzina la Chauta. Tikufunirani madalitso ochokera m'nyumba ya Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Wodala amene akubwera mʼdzina la Yehova. Tikukudalitsani kuchokera ku nyumba ya Yehova. Onani mutuwo |