Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 118:25 - Buku Lopatulika

25 Tikupemphani, Yehova, tipulumutseni tsopano; tikupemphani, Yehova, tipindulitseni tsopano.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Tikupemphani, Yehova, tipulumutseni tsopano; tikupemphani, Yehova, tipindulitseni tsopano.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 Tipulumutseni, tikukupemphani Inu Chauta. Chauta, tikukupemphani kuti zinthu zitiyendere bwino.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Inu Yehova, tipulumutseni; Yehova, tipambanitseni.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 118:25
5 Mawu Ofanana  

Yehova, pulumutsani, mfumuyo ativomereze tsiku lakuitana ife.


ndipulumutseni m'kamwa mwa mkango; inde mwandiyankha ine ndili pa nyanga za njati.


Ndipulumutseni Mulungu; pakuti madzi afikira moyo wanga.


Koma ine, pemphero langa lili kwa Inu, Yehova, m'nyengo yolandirika; Mulungu, mwa chifundo chanu chachikulu, mundivomereze ndi choonadi cha chipulumutso chanu.


Ndipo chisomo chake cha Ambuye Mulungu wathu chikhalire pa ife; ndipo mutikhazikitsire ife ntchito ya manja athu; inde, ntchito ya manja athu muikhazikitse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa