Masalimo 118:27 - Buku Lopatulika27 Yehova ndiye Mulungu, amene anatiunikira; mangani nsembe ndi zingwe, kunyanga za guwa la nsembe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Yehova ndiye Mulungu, amene anatiunikira; mangani nsembe ndi zingwe, kunyanga za guwa la nsembe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Chauta ndi Mulungu, ndipo watipatsa kuŵala. Yambani mdipiti wachikondwerero mutatenga nthambi, mpaka kukafika ku guwa lansembe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Yehova ndi Mulungu, ndipo kuwala kwake kwatiwunikira Ife. Lowani nawo pa mʼdipiti wa ku chikondwerero mutanyamula nthambi mʼdzanja lanu, mpaka ku nyanga za guwa. Onani mutuwo |