Masalimo 118:22 - Buku Lopatulika22 Mwala umene omangawo anaukana wakhala mutu wa pangodya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Mwala umene omangawo anaukana wakhala mutu wa pangodya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Mwala umene amisiri omanga nyumba adaukana, womwewo wasanduka mwala wapangodya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Mwala umene amisiri omanga nyumba anawukana wasanduka wapangodya; Onani mutuwo |