Masalimo 118:21 - Buku Lopatulika21 Ndidzakuyamikani, popeza munandiyankha, ndipo munakhala chipulumutso changa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ndidzakuyamikani, popeza munandiyankha, ndipo munakhala chipulumutso changa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Ndikukuyamikani popeza kuti mwandiyankha, ndipo mwasanduka Mpulumutsi wanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Ndidzakuyamikani chifukwa Inu munandiyankha; mwakhala chipulumutso changa. Onani mutuwo |