Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 118:20 - Buku Lopatulika

20 Chipata cha Yehova ndi ichi; olungama adzalowamo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Chipata cha Yehova ndi ichi; olungama adzalowamo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Ichi ndicho chipata cha Chauta, anthu okhawo ochita chifuniro chake adzaloŵera pamenepa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Ichi ndicho chipata cha Yehova chimene olungama mtima okha adzalowerapo.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 118:20
7 Mawu Ofanana  

Weramutsani mitu yanu, zipata inu; ndipo kwezekani inu, zitseko zosatha, kuti Mfumu ya ulemerero ilowe.


Weramutsani mitu yanu, zipata inu; inde weramutsani, zitseko zosatha inu, kuti Mfumu ya ulemerero ilowe.


Tsegulani pazipata, kuti mtundu wolungama, umene uchita zoonadi, ulowemo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa