Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 118:23 - Buku Lopatulika

23 Ichi chidzera kwa Yehova; nchodabwitsa ichi pamaso pathu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Ichi chidzera kwa Yehova; nchodabwitsa ichi pamaso pathu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Chauta ndiye amene wachita zimenezi, zimenezi nzodabwitsa pamaso pathu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Yehova ndiye wachita zimenezi ndipo nʼzodabwitsa pamaso pathu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 118:23
8 Mawu Ofanana  

amene achita zazikulu ndi zosalondoleka, zinthu zodabwitsa zosawerengeka.


Ichinso chifumira kwa Yehova wa makamu, uphungu wake uzizwitsa ndi nzeru yake impambana.


Taonani, opeputsa inu, zizwani, kanganukani; kuti ndigwiritsa ntchito Ine masiku anu, ntchito imene simudzaikhulupirira wina akakuuzani.


Koma pakuona kulimbika mtima kwa Petro ndi Yohane, ndipo pozindikira kuti ndiwo anthu osaphunzira ndi opulukira, anazizwa ndipo anawazindikira, kuti adakhala pamodzi ndi Yesu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa