Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 118:18 - Buku Lopatulika

18 Kulanga anandilangadi Yehova: koma sanandipereke kuimfa ai.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Kulanga anandilangadi Yehova: koma sanandipereke kuimfa ai.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Chauta wandilanga koopsa, koma sadandisiye kuti ndife.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Yehova wandilanga koopsa, koma sanandipereke ku imfa.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 118:18
14 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake tsono lupanga silidzachoka pa nyumba yako nthawi zonse, popeza unandipeputsa Ine, nudzitengera mkazi wa Uriya Muhiti akhale mkazi wako.


Adzakuombola kuimfa m'njala, ndi kumphamvu ya lupanga m'nkhondo.


Ndinatsikira kumatsinde a mapiri, mipingiridzo ya dziko inanditsekereza kosatha; koma munandikwezera moyo wanga kuuchotsa kuchionongeko, Yehova Mulungu wanga.


Koma poweruzidwa, tilangidwa ndi Ambuye, kuti tingatsutsidwe pamodzi ndi dziko lapansi.


monga osadziwika, angakhale adziwika bwino; monga alinkufa, ndipo taonani tili ndi moyo; monga olangika, ndipo osaphedwa;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa