Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 118:16 - Buku Lopatulika

16 Dzanja lamanja la Yehova likwezeka, Dzanja lamanja la Yehova lichita mwamphamvu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Dzanja lamanja la Yehova likwezeka, Dzanja lamanja la Yehova lichita mwamphamvu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 dzanja lamanja la Chauta lapambana, dzanja lamanja la Chauta limagonjetsa mwamphamvu.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Dzanja lamanja la Yehova latukulidwa mmwamba Dzanja lamanja la Yehova lachita zamphamvu!”

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 118:16
2 Mawu Ofanana  

Dzanja lanu lamanja, Yehova, lalemekezedwa ndi mphamvu, dzanja lanu lamanja, Yehova, laphwanya mdani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa