Masalimo 118:15 - Buku Lopatulika15 M'mahema a olungama muli liu lakufuula mokondwera Dzanja lamanja la Yehova ndi la chipulumutso: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 M'mahema a olungama muli liu lakufuula mokondwera Dzanja lamanja la Yehova ndi la chipulumutso: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Mverani nyimbo m'mahema mwa anthu a Mulungu, nyimbo zokondwerera kupambana, zakuti, “Dzanja lamanja la Chauta limagonjetsa mwamphamvu, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Mfuwu wachimwemwe ndi chipambano ukumveka mʼmatenti a anthu olungama mtima kuti: “Dzanja lamanja la Yehova lachita zamphamvu! Onani mutuwo |