Masalimo 118:12 - Buku Lopatulika12 Adandizinga ngati njuchi; anazima ngati moto waminga; indedi, m'dzina la Yehova ndidzawaduladula. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Adandizinga ngati njuchi; anazima ngati moto waminga; indedi, m'dzina la Yehova ndidzawaduladula. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Adandizinga ngati njuchi, koma adatha msanga ngati moto wapaminga. Ndidaŵaononga ndi mphamvu za dzina la Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Anandizinga ngati njuchi, koma anatha msanga ngati moto wapaminga; mʼdzina la Yehova ndinawawononga. Onani mutuwo |