Masalimo 117:2 - Buku Lopatulika2 Pakuti chifundo chake cha pa ife ndi chachikulu; ndi choonadi cha Yehova nchosatha. Aleluya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Pakuti chifundo chake cha pa ife ndi chachikulu; ndi choonadi cha Yehova nchosatha. Aleluya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Pakuti chikondi chake kwa ife nchachikulu, kukhulupirika kwa Chauta nkwamuyaya. Tamandani Chauta! Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Pakuti chikondi chake pa ife ndi chachikulu, ndipo kukhulupirika kwa Yehova nʼkosatha. Tamandani Yehova. Onani mutuwo |