Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -

Masalimo 117 - Buku Lopatulika


Alemekezedwe Mulungu pa chifundo chake

1 Lemekezani Yehova, amitundu onse; muimbireni, anthu onse.

2 Pakuti chifundo chake cha pa ife ndi chachikulu; ndi choonadi cha Yehova nchosatha. Aleluya.

Bible Society of Malawi

Bible Society of Malawi
Titsatireni:



Zotsatsa