Masalimo 115:8 - Buku Lopatulika8 Adzafanana nao iwo akuwapanga; ndi onse akuwakhulupirira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Adzafanana nao iwo akuwapanga; ndi onse akuwakhulupirira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Anthu amene amapanga mafanowo amafanafana nawo, chimodzimodzi onse amene amaŵakhulupirira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Anthu amene amapanga mafanowo adzafanana nawo, chimodzimodzinso onse amene amadalira mafanowo. Onani mutuwo |