Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 115:5 - Buku Lopatulika

5 Pakamwa ali napo, koma osalankhula; maso ali nao, koma osapenya;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Pakamwa ali napo, koma osalankhula; maso ali nao, koma osapenya;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Pakamwa ali napo, koma salankhula. Maso ali nawo, koma sapenya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Pakamwa ali napo koma sayankhula, maso ali nawo koma sapenya;

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 115:5
2 Mawu Ofanana  

Mafanowa akunga mtengo wakanjedza, wosemasema, koma osalankhula; ayenera awanyamule, pakuti sangathe kuyenda. Musawaope; pakuti sangathe kuchita choipa, mulibenso mwa iwo kuchita chabwino.


Anthu onse ali opulukira ndi opanda nzeru; wakusula golide achitidwa manyazi ndi fanizo lake losema; pakuti fanizo lake loyenga lili bodza, mulibe mpweya m'menemo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa