Masalimo 115:12 - Buku Lopatulika12 Yehova watikumbukira; adzatidalitsa: adzadalitsa nyumba ya Israele; adzadalitsa nyumba ya Aroni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Yehova watikumbukira; adzatidalitsa: adzadalitsa nyumba ya Israele; adzadalitsa nyumba ya Aroni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Chauta watikumbukira ndipo adzatidalitsa. Adzadalitsa anthu a Israele, adzadalitsa banja la Aroni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Yehova watikumbukira ndipo adzatidalitsa: adzadalitsa nyumba ya Israeli, adzadalitsa nyumba ya Aaroni, Onani mutuwo |