Masalimo 112:8 - Buku Lopatulika8 Mtima wake ngwochirikizika, sadzachita mantha, kufikira ataona chofuna iye pa iwo omsautsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Mtima wake ngwochirikizika, sadzachita mantha, kufikira ataona chofuna iye pa iwo omsautsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Ali wolimba mtima, sadzachita mantha, potsiriza adzaona adani ake atagonja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Mtima wake ndi wotetezedwa, sadzakhala ndi mantha; potsiriza pake adzayangʼana adani ake mwachipambano. Onani mutuwo |