Masalimo 112:5 - Buku Lopatulika5 Wodala munthu wakuchitira chifundo, nakongoletsa; adzalimbika nao mlandu wake poweruzidwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Wodala munthu wakuchitira chifundo, nakongoletsa; adzalimbika nao mlandu wake poweruzidwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Munthu amene amakongoza mosafuna phindu, amene amayendetsa ntchito zake mwachilungamo, zinthu zimamuyendera bwino. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Zinthu zabwino zidzabwera kwa iye amene amapereka mowolowamanja ndi wokongoletsa mwaufulu, amene amachita ntchito yake mwachilungamo. Onani mutuwo |