Masalimo 110:4 - Buku Lopatulika4 Yehova walumbira, ndipo sadzasintha, Inu ndinu wansembe kosatha monga mwa chilongosoko cha Melkizedeki. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Yehova walumbira, ndipo sadzasintha, Inu ndinu wansembe kosatha monga mwa chilongosoko cha Melkizedeki. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Chauta walumbira ndipo sadzasintha maganizo ake akuti, “Ndiwe wansembe mpaka muyaya, unsembe wake wonga uja wa Melkizedeki.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Yehova walumbira ndipo sadzasintha maganizo ake: “Ndiwe wansembe mpaka muyaya monga mwa unsembe wa Melikizedeki.” Onani mutuwo |