Masalimo 110:3 - Buku Lopatulika3 Anthu anu adzadzipereka eni ake tsiku la chamuna chanu: M'moyera mokometsetsa, mobadwira matanda kucha, muli nao mame a ubwana wanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Anthu anu adzadzipereka eni ake tsiku la chamuna chanu: M'moyera mokometsetsa, mobadwira matanda kucha, muli nao mame a ubwana wanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Anthu ako adzadzipereka mwaufulu, pa tsiku limene udzaonetse mphamvu zako pa phiri loyera. Anyamata ako adzabwera kwa iwe mu unyinji wao, monga m'mene mame amabwerera m'mamaŵa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Ankhondo ako adzakhala odzipereka pa tsiku lako la nkhondo. Atavala chiyero chaulemerero, kuchokera mʼmimba ya mʼbandakucha, udzalandira mame a unyamata wako. Onani mutuwo |