Masalimo 110:2 - Buku Lopatulika2 Yehova adzatumiza ndodo ya mphamvu yanu kuchokera ku Ziyoni; chitani ufumu pakati pa adani anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Yehova adzatumiza ndodo ya mphamvu yanu kuchokera ku Ziyoni; chitani ufumu pakati pa adani anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Chauta adzakuza ufumu wako wamphamvu kuchokera ku Ziyoni. Adzati, “Khala mfumu yolamulira adani ako.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Yehova adzakuza ndodo yamphamvu ya ufumu wako kuchokera mʼZiyoni; udzalamulira pakati pa adani ako. Onani mutuwo |