Masalimo 11:7 - Buku Lopatulika7 Pakuti Yehova ndiye wolungama; akonda zolungama; woongoka mtima adzapenya nkhope yake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Pakuti Yehova ndiye wolungama; akonda zolungama; woongoka mtima adzapenya nkhope yake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Paja Chauta ndi wolungama, amakonda ntchito zolungama, ndipo anthu olungama adzaona nkhope yake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Pakuti Yehova ndi wolungama, Iye amakonda chilungamo; ndipo anthu olungama adzaona nkhope yake. Onani mutuwo |