Masalimo 11:6 - Buku Lopatulika6 Adzagwetsa pwatapwata misampha pa oipa; moto ndi miyala ya sulufure, ndi mphepo yoopsa zidzawagawikira m'chikho chao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Adzagwetsa pwatapwata misampha pa oipa; moto ndi miyala ya sulufure, ndi mphepo yoopsa zidzawagawikira m'chikho chao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Iye adzaŵagwetsera makala ndi miyala yamoto ngati mvula, adzaŵalanga ndi mphepo yotentha monga kuŵayenera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Iye adzakhuthulira pa oyipa makala amoto ndi sulufule woyaka; mphepo yotentha idzakhala yowayenera. Onani mutuwo |