Masalimo 11:5 - Buku Lopatulika5 Yehova ayesa wolungama mtima, koma moyo wake umuda woipa ndi iye wakukonda chiwawa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Yehova ayesa wolungama mtima, koma moyo wake umuda woipa ndi iye wakukonda chiwawa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Chauta amayesa anthu olungama namakondwera nawo, mtima wake umadana ndi anthu oipa okonda zachiwawa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Yehova amayesa olungama, koma moyo wake umadana ndi oyipa, amene amakonda zachiwawa. Onani mutuwo |