Masalimo 108:4 - Buku Lopatulika4 Pakuti chifundo chanu nchachikulu kupitirira kumwamba, ndi choonadi chanu kufikira mitambo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Pakuti chifundo chanu nchachikulu kupitirira kumwamba, ndi choonadi chanu kufikira mitambo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 pakuti chikondi chanu chosasinthika nchachikulu, chofika mpaka pamwamba pa mlengalenga, kukhulupirika kwanu kumafika mpaka ku mitambo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Pakuti chikondi chanu nʼchachikulu, kutalika kwake kuposa kumwamba; kukhulupirika kwanu kumafika mlengalenga. Onani mutuwo |