Masalimo 108:3 - Buku Lopatulika3 Ndidzakuyamikani mwa mitundu ya anthu, Yehova: ndipo ndidzaimba zakukulemekezani mwa anthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndidzakuyamikani mwa mitundu ya anthu, Yehova: ndipo ndidzaimba zakukulemekezani mwa anthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Ndidzakuthokozani, Inu Chauta, pakati pa mitundu ya anthu. Ndidzaimba nyimbo zokutamandani pakati pa anthu a m'maiko onse, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Ndidzakutamandani Yehova, pakati pa anthu a mitundu ina; ndidzayimba za Inu pakati pa anthu a mitundu ina. Onani mutuwo |