Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 108:10 - Buku Lopatulika

10 Adzandifikitsa ndani m'mzinda wa m'linga? Adzanditsogolera ndani ku Edomu?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Adzandifikitsa ndani m'mudzi wa m'linga? Adzanditsogolera ndani ku Edomu?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Ndani adzandifikitse ku mzinda wamalinga? Ndani adzanditsogolere ku Edomu?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Ndani adzandifikitsa ku mzinda wotetezedwa? Ndani adzanditsogolera ku Edomu?

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 108:10
5 Mawu Ofanana  

Mwatitaya Mulungu, mwatipasula; mwakwiya; tibwezereni.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa