Masalimo 102:28 - Buku Lopatulika28 Ana a atumiki anu adzakhalitsa, ndi mbeu zao zidzakhazikika pamaso panu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Ana a atumiki anu adzakhalitsa, ndi mbeu zao zidzakhazikika pamaso panu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Ana a ife atumiki anu adzakhala opanda nkhaŵa, zidzukulu zathu zidzakhazikika pamaso panu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Ana a atumiki anu adzakhala pamaso panu; zidzukulu zawo zidzakhazikika pamaso panu.” Onani mutuwo |